Eksodo 33:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, ngati ndapeza ufulu pamaso panu, mundidziwitsetu njira zanu, kuti ndikudziweni, ndi kuti ndipeze ufulu pamaso panu; ndipo penyani kuti mtundu uwu ndi anthu anu.

Eksodo 33

Eksodo 33:6-20