Eksodo 31:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Ine, taona, ndampatsa Aholiabu, mwana wa Ahisama, wa pfuko la Dani, akhale naye; ndipo ndaika luso m'mitima ya onse a mtima waluso, kuti apange zonse ndakuuza iwe;

Eksodo 31

Eksodo 31:1-13