Eksodo 30:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene uwerenga ana a Israyeli, monga mwa mawerengedwe ao, munthu yense apereke kwa Yehova ciombolo ca pa moyo wace, pa kuwerengedwa iwowa; kuti pasakhale mliri pakati pao, pakuwerengedwa iwowa.

Eksodo 30

Eksodo 30:2-22