Eksodo 18:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Yetero, Woyamikika Yehova, amene anakulanditsani m'dzanja la Aaigupto, ndi m'dzanja la Farao; ameneanalanditsa anthu awa pansi pa dzanja la Aaigupto.

Eksodo 18

Eksodo 18:1-15