20. Ndipo anacokera ku Sukoti, nagona ku Etamu, pa malekezero a cipululu.
21. Ndipo Yehova anawatsogolera usana ndi mtambo njo kuwatsogolera m'njira; ndi usiku ndi moto njo, wakuwawalitsira; kuti ayende usana ndi usiku;
22. sanacotsa mtambo usana, kapena mtambo wamoto usiku, pamaso pa anthu.