Eksodo 11:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma palibe garu adzafunyitsira lilime lace ana onse a Israyeli ngakhale anthu kapena zoweta; kuti mudziwe kuti Yehova asiyanitsa pakati pa Aaigupto ndi Aisrayeli.

Eksodo 11

Eksodo 11:2-10