Deuteronomo 9:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndinacita mantha cifukwa ca mkwiyo waukali, umene Yehova anakwiya nao pa inu kukuonongani, Koma Yehova anandimvera nthawi ijanso.

Deuteronomo 9

Deuteronomo 9:18-21