Deuteronomo 4:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova anakwiyanso nane cifukwa ca mau anu, nalumbira kuti sindidzaoloka Yordano ine, ndi kuti sindidzalowa m'dziko lokomali Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale colowa canu;

Deuteronomo 4

Deuteronomo 4:17-29