Deuteronomo 3:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndinapatsa Arubeni ndi Agadi kuyambira ku Gileadi kufikira ku mtsinje wa Arinoni, pakati pa cigwa ndi malire ace, kufikira mtsinje wa Yaboki, ndiwo malire a ana a Amoni;

Deuteronomo 3

Deuteronomo 3:10-26