Deuteronomo 29:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kungakhale, akamva mau a lumbiro ili adzadzidalitsa m'mtima mwace, ndi kuti, Ndidzakhala nao mtendere, ndingakhale ndiyenda nao mtima wanga wopulukira, kuledzera nditamva ludzu;

Deuteronomo 29

Deuteronomo 29:13-25