Deuteronomo 28:55 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

osapatsako mmodzi yense wa iwowa nyama ya ana ace alinkudyayo, popeza sikamtsalira kanthu; pakukumangirani tsasa ndi kukupsinjani mdani wanu m'midzi mwanu monse.

Deuteronomo 28

Deuteronomo 28:46-64