Deuteronomo 28:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova adzalola adani anu akukantheni; mudzawaturukira njira imodzi, koma mudzawathawa pamaso pao njira zisanu ndi ziwiri, ndipo mudzagwedezeka pakati pa maufumu onse a dziko lapansi.

Deuteronomo 28

Deuteronomo 28:20-32