Deuteronomo 22:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo azimturutsa namwaliyo ku khomo la nyumba ya atate wace, ndipo amuna a mudzi wace azimponya miyala kuti afe; popeza anacita copusa m'Israyeli, kucita cigololo m'nyumba ya atate wace; cotero uzicotsa coipaco pakati panu.

Deuteronomo 22

Deuteronomo 22:13-29