Deuteronomo 22:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi kumlipitsa masekeli makumi okha okha khumi a siliva, ndi kuipereka kwa atate wa namwaliyo, popeza anamveketsa dzina loipa namwali wa Israyeli, ndipo azikhala mkazi wace, sakhoza kumcotsa masiku ace onse.

Deuteronomo 22

Deuteronomo 22:15-29