Deuteronomo 21:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo kudzali, tsiku lakugawira ana ace amuna cuma cace, sangakhoze kuyesa mwana wa wokondana naye woyamba kubadwa, wosati mwana wa wodana naye, ndiye woyamba kubadwatu.

Deuteronomo 21

Deuteronomo 21:15-22