Deuteronomo 2:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Sihoni mfumu ya Hesiboni sanatilola kupitira kwao; popeza Yehova Mulungu wanu anaumitsa mzimu wace, nalimbitsa mtima wace, kuti ampereke m'dzanja lanu, monga lero lino.

Deuteronomo 2

Deuteronomo 2:25-37