Deuteronomo 2:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene uyandikiza popenyana ndi ana a Amoni, usawabvuta, kapena kuutsana nao; popeza sindidzakupatsako dziko la ana a Amoni likhale lako lako; popeza ndinapatsa ana a Loti ili likhale lao lao.

Deuteronomo 2

Deuteronomo 2:12-26