Deuteronomo 12:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mudzaoloka Yordano, ndi kukhala m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akulandiritsani; ndipo adzakupumulitsani akulekeni adani anu onse pozungulirapo, ndipo mudzakhala mokhazikika.

Deuteronomo 12

Deuteronomo 12:1-16