Cibvumbulutso 8:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo dzina lace la nyenyeziyo alicha Cowawa; ndipo limodzi la magawo atatu a madzi lidasanduka cowawa; ndipo anthu ambiri adafa pakumwa madzi, pakuti anasanduka owawa.

Cibvumbulutso 8

Cibvumbulutso 8:5-12