Cibvumbulutso 6:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinaona pamene anamasula cizindikilo cacisanu ndi cimodzi, ndipo panali cibvomezi cacikuru; ndi dzuwa lidada bii longa ciguduli ca ubweya ndi mwezi wonse unakhala ngati mwazi;

Cibvumbulutso 6

Cibvumbulutso 6:2-17