Cibvumbulutso 22:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ine Yohane ndine wakumva ndi wakupenya izi. Ndipo pamene ndinamva ndi kupenya, ndinagwa pansi kulambira pa mapazi a mngelo wakundionetsa izo.

Cibvumbulutso 22

Cibvumbulutso 22:7-15