Cibvumbulutso 22:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo sikudzakhalanso usiku; ndipo sasowa kuunika kwa nyali, ndi kuunika kwa dzuwa; cifukwa Ambuye Mulungu adzawaunikira; ndipo adzacita ufumu ku nthawi za nthawi.

Cibvumbulutso 22

Cibvumbulutso 22:1-14