Cibvumbulutso 22:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye wakukhala wosalungama acitebe zosalungama; ndi munthu wonyansa akhalebe wonyansa; ndi iye wakukhala wolungama acitebe colungama; ndi iye amene ali woyera akhalebe woyeretsedwa.

Cibvumbulutso 22

Cibvumbulutso 22:8-13