Cibvumbulutso 21:26-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)
26. ndipo 5 adzatenga ulemerero ndi ulemu wa amitundu nadzalowa nao momwemo;
27. ndipo 6 simudzalowa konse momwemo kanthu kali konse kosapatulidwa kapena iye wakucita conyansa ndi bodza; koma iwo okha olembedwa 7 m'buku la moyo la Mwanawankhosa.