Cibvumbulutso 21:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo 1 pamzinda sipafunika dzuwa, kapena mwezi wakuuwalira; pakuti ulemerero wa Mulungu uunikira umenewu, ndipo nyali yace ndiye Mwanawankhosa.

Cibvumbulutso 21

Cibvumbulutso 21:22-27