Cibvumbulutso 20:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nadzaturuka kudzasokeretsa amitundu ali mu ngondya zinai za dziko, Gogo, ndi Magogo, kudzawasonkhanitsa acite nkhondo: ciwerengero cao ca iwo amene cikhala ngati mcenga wa kunyanja.

Cibvumbulutso 20

Cibvumbulutso 20:5-9