Cibvumbulutso 19:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo m'kamwa mwace muturuka Iupanga lakuthwa, kuti akanthe nalo mitundu ya anthu; ndipo iye adzawalamulira ndi ndodo yacitsulo: ndipo aponda iye moponderamo mphesa mwa vinyo waukali wa mkwiyo wa Mulungu Wamphamvuyonse.

Cibvumbulutso 19

Cibvumbulutso 19:5-16