Cibvumbulutso 17:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinaona mkazi woledzera ndi mwazi wa oyera mtima, ndi mwazi wa mboni za Yesu; ndipo ndinazizwa pakumuona iye ndi kuzizwa kwakukuru.

Cibvumbulutso 17

Cibvumbulutso 17:1-16