Cibvumbulutso 17:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ananditenga kumka nane kucipululu, mu Mzimu; ndipo ndinaona mkazi alinkukhala pacirombo cofiiritsa, codzala ndi maina a mwano, cakukhala nayo mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi.

Cibvumbulutso 17

Cibvumbulutso 17:1-12