Cibvumbulutso 15:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Kacisi anadzazidwa ndi utsi wocokera ku ulemerero wa Mulungu ndi ku mphamvu yace; ndipo palibe munthu anakhoza kulowa m'Kacisi kufikira ikatha miliri isanu ndi iwiri ya angelo asanu ndi awiri.

Cibvumbulutso 15

Cibvumbulutso 15:1-8