Cibvumbulutso 15:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndani adzakhala wosaopa ndi wosalemekeza dzina lanu Ambuye? Cifukwa Inu nokha muli woyera; cifukwa mitundu yonse idzadza nidzalambira pamaso panu, popeza zolungama zanu zidaonetsedwa.

Cibvumbulutso 15

Cibvumbulutso 15:1-7