Cibvumbulutso 10:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

komatu m'masiku a mau a mngelo wacisanu ndi ciwiri m'mene iye adzayamba kuomba, pamenepo padzatsirizika cinsinsi ca Mulungu, monga analalikira kwa akapolo ace aneneri.

Cibvumbulutso 10

Cibvumbulutso 10:1-11