12. cotero kunanenedwa kwa uyo, Wamkuru adzakhala kapolo wa wamng'ono.
13. Inde monga kunalembedwa, Ndinakonda Yakobo, koma ndinamuda Esau.
14. Ndipo tsono tidzatani? Kodi ciripo cosalungama ndi Mulungu? Msatero ai.
15. Pakuti anati ndi Mose, Ndidzacitira cifundo amene ndimcitira cifundo, ndipo ndidzakhala ndi cisoni kwa iye amene ndikhala naye cisoni.