Aroma 8:19-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Pakuti ciyembekezetso ca colengedwa cilimilia bvumbulutso la ana a Molungu.

20. Pakuti colengedwaco cagonietsedwa kuutsiru, cosafuna mwini, koma cifukwa ca iye amene anacigonjetsa,

21. ndi ciyembekezo kuti colengedwa comwe cidzamasulidwa ku ukapolo wa cibvundi, ndi kolowa ufulu wa ulemerero wa ana a Mulungu,

Aroma 8