Aroma 2:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace uli wopanda mau owiringula, munthu iwe, amene uli yense wakuweruza; pakuti m'mene uweruza wina, momwemo udzitsutsa iwe wekha, pakuti iwe wakuweruza, umacita zomwezo.

Aroma 2

Aroma 2:1-5