Aroma 16:20-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Ndipo Mulungu wa mtendere adzaphwanva: Satana pansi pa mapazi anu tsopano lino.Cisomo ca Ambuye wathu Yesu Kristu cikhale ndi inu nonse.

21. Timoteo wanchito mnzanga akulankhulani inu; ndi Lukiyo ndi Yasoni ndi Sosipatro, abale anga.

22. Ine Tertio, ndirikulemba kalata ameneyu, ndikulankhulani inu mwa Ambuye.

Aroma 16