Aroma 14:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye wakusamalira tsiku, alisamalira kwa Ambuye: ndipo iye wakudya, adya mwa Ambuye, pakuti ayamika Mulungu; ndipo iye wosadya, mwa Ambuye sakudya, nayamikanso Mulungu.

Aroma 14

Aroma 14:4-8