Aroma 11:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ngati nthambi zina zinathyoledwa, ndipo iwe, ndiwe mtengo wazitona wa kuthengo, unamezetsanidwa mwa izo, nugawana nazo za muzu za mafuta ace a mtengowo,

Aroma 11

Aroma 11:7-25