Aroma 1:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa ca ici Mulungu anawapereka iwo 1 ku zilakolako za manyazi; pakuti angakhale akazi ao anasandutsa macitidwe ao a cibadwidwe akhale macitidwe osalingana ndi cibadwidwe:

Aroma 1

Aroma 1:25-28