Amosi 9:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kodi simukhala kwa Ine ngati ana a Kusi, inu ana a Israyeli? ati Yehova. Sindinakweza Israyeli ndine, kumturutsa m'dziko la Aigupto, ndi Afilisti ku Kafitori, ndi Aaramu ku Kiri?

Amosi 9

Amosi 9:5-15