Amosi 7:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunacitika m'mene lidatha kudya msipu wa dziko, ndinati, Ambuye Yehova, khululukiranitu Yakobo; adzakhala ciriri bwanji? popeza ndiye wamng'ono.

Amosi 7

Amosi 7:1-7