Amosi 4:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndinagubuduza ena mwa inu, monga umo Mulungu anagubuduzira Sodomu ndi Gomora; ndipo inu munali ngati muuni wofumulidwa kumoto; koma simunabwerera kudza kwa Ine, ati Yehova.

Amosi 4

Amosi 4:6-13