Ahebri 7:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Ndipo pano anthu ofeka alandira limodzi la magawo khumi; koma apo iye, woti adamcitira umboni kuti ali ndi moyo.

9. Ndipo kuli ngati kunena, mwa Abrahamu Levinso wakulandira limodzi limodzi la magawo khumi adapereka limodzi la magawo khumi;

10. pakuti pajapo anali m'cuuno ca atate wace, pamene Melikizedeke anakomana naye.

Ahebri 7