9. ndipo pamene anakonzeka wamphumphu anakhala kwa onse akumvera iye cifukwa ca cipulumutso cosatha;
10. wochedwa ndi Mulungu mkulu wa ansembe monga mwa dongosolo la Melikizedeke.
11. Za iye tirinao mau ambiri kuwanena, ndiotilaka powatanthauzira, popeza mwagontha m'makutu.