Ahebri 5:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. ndipo pamene anakonzeka wamphumphu anakhala kwa onse akumvera iye cifukwa ca cipulumutso cosatha;

10. wochedwa ndi Mulungu mkulu wa ansembe monga mwa dongosolo la Melikizedeke.

11. Za iye tirinao mau ambiri kuwanena, ndiotilaka powatanthauzira, popeza mwagontha m'makutu.

Ahebri 5