Ahebri 4:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti kwa ifenso walalikidwa Uthenga Wabwino, monganso kwa iwo; koma iwowa sanapindula nao mau omvekawo, popeza sanasanganizika ndi cikhulupiriro mwa iwo amene adawamva.

Ahebri 4

Ahebri 4:1-3