Ahebri 12:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Komanso, tinali nao atate a thupi lathu akutilanga, ndipo tinawalemekeza; kodi sitidzagonjera Atate wa mizimu koposa nanga, ndi kukhala ndi moyo?

Ahebri 12

Ahebri 12:1-15