14. Pakuti ndi cipereko cimodzi anawayesera angwiro cikhalire iwo oyeretsedwa.
15. Koma Mzimu Woyeranso aticitira umboni; pakuti adatha kunena,
16. ici ndi cipangano ndidzapangana nao,Atapira masiku ajawo, anena Ambuye:Ndidzapereka malamulo anga akhale pamtima pao;Ndipo pa nzeru zao ndidzawalemba;
17. Ndipo macimo ao ndi masayeruziko ao sindidzawakumbukilanso.