Afilipi 4:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Koma munacita bwino kuti munayanjana nane m'cisautso canga.

15. Koma mudziwanso inu nokha, inu Afilipi, kuti m'ciyambi ca Uthenga Wabwino, pamene ndinacoka kuturuka m'Makedoniya, sunayanjana nane Mpingo umodzi wonse m'makhalidwe a copereka ndi colandira; koma inu nokha;

16. pakuti m'Tesalonikanso munanditumizira pa cosowa canga kamodzi kapena kawiri.

Afilipi 4