Aefeso 6:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akapolo inu, mverani iwo amene ali ambuye anu monga mwa thupi, ndi kuwaopa ndi kunthunthumira nao, ndi mtima wanu wosakumbukila kanthu kena, monga kwa Kristu;

Aefeso 6

Aefeso 6:1-10