Aefeso 6:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ananu, mverani akukubalani mwa Ambuye, pakuti ici ncabwino.

2. Lemekeza atate wako ndi amako (ndilo lamulo loyamba lokhala nalo lonjezano),

3. kuti kukhale bwino ndi iwe, ndi kuti ukhale wa nthawi yaikuru padziko.

Aefeso 6